Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chichewa-vertaling - Khalid Ibrahim Beitala

AL-Muddaththir

external-link copy
1 : 74

يَٰٓأَيُّهَا ٱلۡمُدَّثِّرُ

E iwe wadziphimba (nsalu)! info
التفاسير:

external-link copy
2 : 74

قُمۡ فَأَنذِرۡ

Imilira ndipo uwachenjeze (anthu za chilango cha Allah). info
التفاسير:

external-link copy
3 : 74

وَرَبَّكَ فَكَبِّرۡ

Ndipo Mbuye wako (Yekha) umkulitse (pomulemekeza). info
التفاسير:

external-link copy
4 : 74

وَثِيَابَكَ فَطَهِّرۡ

Ndipo nsalu zako uziyeretse (ndi madzi ku uve). info
التفاسير:

external-link copy
5 : 74

وَٱلرُّجۡزَ فَٱهۡجُرۡ

Ndiponso zoipa (monga mafano ndi zina zonse ) zipewe. info
التفاسير:

external-link copy
6 : 74

وَلَا تَمۡنُن تَسۡتَكۡثِرُ

Usapatse (anthu) ncholinga choti ulandire zambiri. info
التفاسير:

external-link copy
7 : 74

وَلِرَبِّكَ فَٱصۡبِرۡ

Chifukwa cha Mbuye wako, pirira (ku malamulo Ake poleka zomwe waletsa ndi kuchita zimene walamula). info
التفاسير:

external-link copy
8 : 74

فَإِذَا نُقِرَ فِي ٱلنَّاقُورِ

Ndipo likadzaimbidwa lipenga, info
التفاسير:

external-link copy
9 : 74

فَذَٰلِكَ يَوۡمَئِذٖ يَوۡمٌ عَسِيرٌ

Tsiku limenelo lidzakhala tsiku lovuta. info
التفاسير:

external-link copy
10 : 74

عَلَى ٱلۡكَٰفِرِينَ غَيۡرُ يَسِيرٖ

Kwa osakhulupirira, silidzakhala lofewa. info
التفاسير:

external-link copy
11 : 74

ذَرۡنِي وَمَنۡ خَلَقۡتُ وَحِيدٗا

Ndisiye ndiamene ndidamlenga Ndekha, info
التفاسير:

external-link copy
12 : 74

وَجَعَلۡتُ لَهُۥ مَالٗا مَّمۡدُودٗا

Ndipo ndampatsa chuma chambiri. info
التفاسير:

external-link copy
13 : 74

وَبَنِينَ شُهُودٗا

Ndi ana okhala nawo (paliponse). info
التفاسير:

external-link copy
14 : 74

وَمَهَّدتُّ لَهُۥ تَمۡهِيدٗا

Ndipo ndamkonzera (ulemelero), kumkonzera (kwabwino). info
التفاسير:

external-link copy
15 : 74

ثُمَّ يَطۡمَعُ أَنۡ أَزِيدَ

Kenako ali ndi dyera kuti ndimuonjezere (zina popanda kuthokoza). info
التفاسير:

external-link copy
16 : 74

كَلَّآۖ إِنَّهُۥ كَانَ لِأٓيَٰتِنَا عَنِيدٗا

Koma sichoncho! Ndithu iye adali kutsutsa zizindikiro Zathu. info
التفاسير:

external-link copy
17 : 74

سَأُرۡهِقُهُۥ صَعُودًا

Ndidzamkakamiza kuchilango chovuta; (kukwera phiri la ku Moto limene sakatha kulikwera). info
التفاسير:

external-link copy
18 : 74

إِنَّهُۥ فَكَّرَ وَقَدَّرَ

Iye adalingalira (mu mtima mwake) ndi kukonza bwino (chonena chonyoza Qur’an). info
التفاسير: