Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chichewa-vertaling - Khalid Ibrahim Beitala

external-link copy
73 : 27

وَإِنَّ رَبَّكَ لَذُو فَضۡلٍ عَلَى ٱلنَّاسِ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَهُمۡ لَا يَشۡكُرُونَ

Ndipo ndithu Mbuye wako ndi mwini kupereka ubwino (waukulu) kwa anthu; koma ambiri a iwo sathokoza. info
التفاسير: