ශුද්ධවූ අල් කුර්ආන් අර්ථ කථනය - චිචේවා පරිවර්තනය - කාලිද් ඉබ්රාහීම් බීතාලා

Al-Mutaffîfîn

external-link copy
1 : 83

وَيۡلٞ لِّلۡمُطَفِّفِينَ

Kuonongeka koopsa kukawapeza opunguza miyeso ya malonda. info
التفاسير:

external-link copy
2 : 83

ٱلَّذِينَ إِذَا ٱكۡتَالُواْ عَلَى ٱلنَّاسِ يَسۡتَوۡفُونَ

Amene amati akamadziyezera zinthu kwa anthu amafuna kulandira miyeso yodzadza. info
التفاسير:

external-link copy
3 : 83

وَإِذَا كَالُوهُمۡ أَو وَّزَنُوهُمۡ يُخۡسِرُونَ

Koma pamene iwo akamawayesera pa muyeso wa mbale kapena wa sikelo amapungula (choyenera kulandira ogulawo). info
التفاسير:

external-link copy
4 : 83

أَلَا يَظُنُّ أُوْلَٰٓئِكَ أَنَّهُم مَّبۡعُوثُونَ

Kodi amenewa (akupungula miyeso pamalondawo) sakuganiza kuti adzaukitsidwa; info
التفاسير: