ترجمهٔ معانی قرآن کریم - ترجمه‌ى چوایی - خالد ابراهیم بيتالا

external-link copy
5 : 97

سَلَٰمٌ هِيَ حَتَّىٰ مَطۡلَعِ ٱلۡفَجۡرِ

Mtendere usiku umenewo! (Palibe mavuto ndi zoipa) mpaka m’bandakucha.[465] info

[465] Adanena Baidawi kuti tanthauzo la Ayah iyi ndikuti mu usiku umenewu Allah amalamula kuti kukhale mtendere wokhawokha. Koma mu usiku wina amalamula kuti kukhale mtendere ndi masoka.

التفاسير: